Nkhuku ndi Bongololo anali abwenzi. Koma anali kukonda kupikisana paiwo okha. Tsiku lina, anaganiza kusewela m’pila wa myendo kuti aone ngati katswili ndani.
Chicken and Millipede were friends. But they were always competing with each other. One day they decided to play football to see who the best player was.
Anayenda kubwalo la m’pila ndipo anayamba masewela awo. Nkhuku inafulumila, koma Bongololo anafulumila kopambana. Nkhuku inapandila kutali koma bongololo anapandila kutali mopambana. Nkhuku inayamba kukalipa.
They went to the football field and started their game. Chicken was fast, but Millipede was faster. Chicken kicked far, but Millipede kicked further. Chicken started to feel grumpy.
They decided to play a penalty shoot-out. First Millipede was goal keeper. Chicken scored only one goal. Then it was the chicken’s turn to defend the goal.
Bongololo anasewela ndipo anamwetsa. Bongololo ananyunya ndi kumwetsa. Bongololo anamwesanso ndi mutu. Bongololo anamwetsa zigoli zisanu.
Millipede kicked the ball and scored.
Millipede dribbled the ball and scored. Millipede headed the ball and scored. Millipede scored five goals.
As Chicken was walking home, she met Mother Millipede. Mother Millipede asked, “Have you seen my child?” Chicken didn’t say anything.
Mother Millipede was worried.
Amake Bongololo anamva timau tating’ono. “Ndithandizeni amai!” liu linalila. Amake Bongololo anayangana uku ndi uku, ndi kumvetsetsa ndi cidwi. Mau anacokela mumimba mwa nkhuku.
Then Mother Millipede heard a tiny voice. “Help me mom!” cried the voice. Mother Millipede looked around and listened carefully. The voice came from inside the chicken.